Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 21:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ahabu anachita zinthu zonyansa kwambiri mwa kutsatira mafano onyansa+ monga momwe Aamori, amene Yehova anawathamangitsa pamaso pa ana a Isiraeli, anachitira.’”+

  • 2 Mafumu 21:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Manase+ mfumu ya Yuda yachita zinthu zonyansazi.+ Yachita zinthu zoipa kwambiri kuposa zonse zimene anachita Aamori+ amene analiko iye asanakhale mfumu. Iye wachimwitsa ngakhale Yuda+ ndi mafano ake onyansa.

  • Ezekieli 16:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Iwe ndiwe mwana wamkazi wa mayi ako,+ omwe amanyansidwa ndi mwamuna wawo+ ndi ana awo aamuna. Ndiwe m’bale wawo wa abale ako, amene amanyansidwa ndi amuna awo ndi ana awo aamuna. Akazi inu, mayi wanu anali Mhiti,+ ndipo bambo wanu anali Muamori.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena