Ekisodo 23:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Komanso muzichita chikondwerero cha zokolola, chokondwerera zipatso za ntchito ya manja anu zoyamba kucha+ zimene munabzala m’munda.+ Muzichitanso chikondwerero cha kututa kumapeto kwa chaka, pamene mututa zipatso za manja anu, zam’munda.+ 1 Samueli 9:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Koma Sauli anafunsa mtumiki wakeyo kuti: “Ndiye tikapita kumeneko tikam’patsa chiyani?+ Tilibe mphatso+ imene tingapatse munthu wa Mulungu woonayo, chifukwanso mkate watha m’zotengera zathu. Tili ndi chiyani?” Agalatiya 6:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Komanso, aliyense amene akuphunzitsidwa mawuwo+ agawane+ zinthu zonse zabwino ndi amene akumuphunzitsayo.+
16 Komanso muzichita chikondwerero cha zokolola, chokondwerera zipatso za ntchito ya manja anu zoyamba kucha+ zimene munabzala m’munda.+ Muzichitanso chikondwerero cha kututa kumapeto kwa chaka, pamene mututa zipatso za manja anu, zam’munda.+
7 Koma Sauli anafunsa mtumiki wakeyo kuti: “Ndiye tikapita kumeneko tikam’patsa chiyani?+ Tilibe mphatso+ imene tingapatse munthu wa Mulungu woonayo, chifukwanso mkate watha m’zotengera zathu. Tili ndi chiyani?”
6 Komanso, aliyense amene akuphunzitsidwa mawuwo+ agawane+ zinthu zonse zabwino ndi amene akumuphunzitsayo.+