Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 82:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Chitirani chilungamo anthu onyozeka ndi ana amasiye.*+

      Chitirani chilungamo anthu osautsika ndi osauka.+

  • Miyambo 21:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mtima wa mfumu uli ngati mitsinje yamadzi m’dzanja la Yehova.+ Amautembenuzira kulikonse kumene iye akufuna.+

  • Miyambo 29:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pochita zinthu zachilungamo, mfumu imachititsa dziko kulimba,+ koma munthu wokonda ziphuphu amaligwetsa.+

  • Miyambo 31:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsegula pakamwa pako, weruza mwachilungamo ndipo thandiza munthu wosautsika ndi wosauka pa mlandu wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena