1 Samueli 9:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Poyankha mtumikiyo anauzanso Sauli kuti: “Inetu ndili ndi gawo limodzi mwa magawo anayi a sekeli*+ la siliva loti ndingam’patse munthu wa Mulungu woonayo ndipo adzatiuza kumene tingalowere.” 1 Mafumu 14:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Utenge mitanda 10 ya mkate,+ makeke, ndi botolo+ la uchi, ndipo ukafike kwa iyeyo.+ Iye ndiye akakuuze zimene zichitikire mnyamatayu.”+ 2 Mafumu 5:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Ndiyeno mfumu ya Siriya inauza Namani kuti: “Nyamuka, ndikupatsa kalata upite kwa mfumu ya Isiraeli.” Choncho iye ananyamuka atatenga+ matalente* 10 a siliva, masekeli 6,000 a golide,+ ndi zovala 10.+
8 Poyankha mtumikiyo anauzanso Sauli kuti: “Inetu ndili ndi gawo limodzi mwa magawo anayi a sekeli*+ la siliva loti ndingam’patse munthu wa Mulungu woonayo ndipo adzatiuza kumene tingalowere.”
3 Utenge mitanda 10 ya mkate,+ makeke, ndi botolo+ la uchi, ndipo ukafike kwa iyeyo.+ Iye ndiye akakuuze zimene zichitikire mnyamatayu.”+
5 Ndiyeno mfumu ya Siriya inauza Namani kuti: “Nyamuka, ndikupatsa kalata upite kwa mfumu ya Isiraeli.” Choncho iye ananyamuka atatenga+ matalente* 10 a siliva, masekeli 6,000 a golide,+ ndi zovala 10.+