Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 13:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 M’chaka cha 23 cha Yehoasi+ mwana wa Ahaziya+ mfumu ya Yuda, Yehoahazi+ mwana wa Yehu+ anakhala mfumu ya Isiraeli ku Samariya, kwa zaka 17.

  • 2 Mafumu 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 M’chaka cha 37 cha Yehoasi+ mfumu ya Yuda, Yehoasi mwana wa Yehoahazi anakhala mfumu ya Isiraeli ku Samariya kwa zaka 16.

  • 2 Mafumu 14:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 M’chaka cha 15 cha Amaziya mwana wa Yehoasi mfumu ya Yuda, Yerobowamu+ mwana wa Yehoasi mfumu ya Isiraeli anakhala mfumu ku Samariya, ndipo analamulira zaka 41.

  • 2 Mafumu 15:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 M’chaka cha 38 cha Azariya+ mfumu ya Yuda, Zekariya+ mwana wa Yerobowamu anakhala mfumu ya Isiraeli ku Samariya kwa miyezi 6.

  • 2 Mafumu 15:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Izi zinakwaniritsa mawu a Yehova+ amene anawalankhula kwa Yehu, akuti:+ “Ana+ ako aamuna adzakhala pampando wachifumu wa Isiraeli mpaka m’badwo wachinayi.” Ndipo zinaterodi.+

  • Yobu 34:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti iye amapereka mphoto kwa munthu wochokera kufumbi malinga ndi zochita zake,+

      Ndipo amam’bweretsera zinthu zogwirizana ndi njira yake.

  • Aheberi 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti Mulungu si wosalungama woti angaiwale ntchito yanu ndi chikondi chimene munachisonyeza pa dzina lake,+ mwa kutumikira oyera+ ndipo mukupitiriza kuwatumikira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena