Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 ndipo Yoswa anawachitira maere pamaso pa Yehova+ ku Silo. Kumeneko Yoswa anagawa dzikolo n’kupereka gawo limodzilimodzi ku mafuko a ana a Isiraeli.+

  • 1 Mbiri 25:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako anachita maere+ powagawira ntchito yoti azichita. Pochita maerewo, onse anali chimodzimodzi. Sanali kuyang’ana kuti uyu ndi wamng’ono kapena wamkulu,+ katswiri+ kapena wophunzira kumene.

  • Miyambo 16:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Maere amaponyedwa pamwendo,+ koma zonse zimene maerewo amasonyeza zimachokera kwa Yehova.+

  • Machitidwe 1:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Atatero anachita maere+ pa iwo, ndipo maerewo anagwera Matiya. Choncho iye anamuphatikiza pa atumwi 11+ aja.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena