Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 6:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndipo ana aamuna a Uziyeli anali Misayeli, Elizafana ndi Sitiri.+

  • Levitiko 10:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Zitatero, Mose anaitana Misayeli ndi Elizafana, ana a Uziyeli,+ bambo aang’ono a Aroni, n’kuwauza kuti: “Bwerani muchotse abale anu patsogolo pa malo oyera, mupite nawo kunja kwa msasa.”+

  • 1 Mbiri 15:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pa ana a Uziyeli+ panali Aminadabu mtsogoleri wawo ndi abale ake okwanira 112.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena