Yoswa 15:42 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 42 Libina,+ Eteri,+ Asani, Yoswa 21:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Ana a wansembe Aroni anawapatsa mzinda wothawirako munthu+ amene wapha mnzake,+ wa Heburoni+ ndi malo ake odyetserako ziweto. Anawapatsanso Libina+ ndi malo ake odyetserako ziweto,
13 Ana a wansembe Aroni anawapatsa mzinda wothawirako munthu+ amene wapha mnzake,+ wa Heburoni+ ndi malo ake odyetserako ziweto. Anawapatsanso Libina+ ndi malo ake odyetserako ziweto,