Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 35:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kwa ana a Isiraeli, kwa mlendo,+ ndi kwa munthu amene wakhaliratu pakati pawo, mizinda 6 imeneyi ikakhala kothawirako aliyense amene wapha munthu mwangozi.+

  • Yoswa 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mizindayo ntchito yake ikhale yoti wopha munthu+ mwangozi azithawirako pothawa wobwezera magazi.+

  • 1 Mbiri 6:57
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 57 Ana a Aroni anawapatsa mzinda* wothawirako+ wa Heburoni,+ mzinda wa Libina+ ndi malo ake odyetserako ziweto, mzinda wa Yatiri,+ mzinda wa Esitemowa+ ndi malo ake odyetserako ziweto,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena