Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 10:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ukachoka pamenepo ufika kuphiri la Mulungu woona,+ kumene kuli mudzi wa asilikali+ a Afilisiti. Ndiyeno zimene zichitike n’zakuti, poyandikira mzindawo, ukumana ndi kagulu ka aneneri+ akuchokera kumalo okwezeka,+ akulankhula monga aneneri. Patsogolo pawo pakhala pali choimbira cha zingwe,+ maseche,+ chitoliro+ ndi zeze.+

  • 1 Samueli 13:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Isiraeli yense anamva anthu akukamba kuti: “Sauli wakantha mudzi wa asilikali a Afilisiti, ndipo tsopano Isiraeli wakhala chinthu chonunkha+ kwa Afilisiti.” Choncho anasonkhanitsa anthu onse pamodzi kuti atsatire Sauli ku Giligala.+

  • 1 Samueli 13:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Tsopano gulu la asilikali+ a Afilisiti linali kutuluka mumsasa ndi kupita kumalo owolokera a ku Mikimasi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena