Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Motero analowetsa+ likasa la Mulungu woona muhema limene Davide anamanga, n’kuika likasalo pamalo ake muhemalo.+ Kenako iwo anapereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano kwa Mulungu woona.+

  • Salimo 132:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Kufikira Yehova nditamupezera nyumba,+

      Kufikira nditapeza chihema chachikulu cha Wamphamvu wa Yakobo.”+

  • Machitidwe 7:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Mulungu anakomera mtima+ Davide ndipo iye anapempha mwayi wakuti amange nyumba yokhalamo+ Mulungu wa Yakobo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena