2 Samueli 7:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 inauza Natani+ mneneri kuti: “Tsopano taona, ine ndikukhala m’nyumba ya mitengo ya mkungudza,+ pamene likasa la Mulungu woona likukhala m’chihema chansalu.”+ 1 Mbiri 15:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndiyeno Davide anasonkhanitsa Aisiraeli onse ku Yerusalemu+ kuti akanyamule likasa+ la Yehova, kupita nalo kumalo amene iye anakonza kuti akaliike. 1 Mbiri 15:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Tsopano Davide anawauza kuti: “Inuyo ndinu atsogoleri+ a nyumba ya makolo a Alevi. Choncho inu ndi abale anu mudziyeretse,+ ndipo mukatenge likasa la Yehova Mulungu wa Isiraeli n’kukaliika kumalo amene ine ndakonza kuti likakhaleko. Machitidwe 7:46 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 46 Mulungu anakomera mtima+ Davide ndipo iye anapempha mwayi wakuti amange nyumba yokhalamo+ Mulungu wa Yakobo.
2 inauza Natani+ mneneri kuti: “Tsopano taona, ine ndikukhala m’nyumba ya mitengo ya mkungudza,+ pamene likasa la Mulungu woona likukhala m’chihema chansalu.”+
3 Ndiyeno Davide anasonkhanitsa Aisiraeli onse ku Yerusalemu+ kuti akanyamule likasa+ la Yehova, kupita nalo kumalo amene iye anakonza kuti akaliike.
12 Tsopano Davide anawauza kuti: “Inuyo ndinu atsogoleri+ a nyumba ya makolo a Alevi. Choncho inu ndi abale anu mudziyeretse,+ ndipo mukatenge likasa la Yehova Mulungu wa Isiraeli n’kukaliika kumalo amene ine ndakonza kuti likakhaleko.
46 Mulungu anakomera mtima+ Davide ndipo iye anapempha mwayi wakuti amange nyumba yokhalamo+ Mulungu wa Yakobo.