Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 10:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano dziwani kuti mawu onse a Yehova otsutsa nyumba ya Ahabu+ amene Yehova analankhula, adzakwaniritsidwa.+ Yehova wachita zimene analankhula kudzera mwa mtumiki wake Eliya.”+

  • 2 Mafumu 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kuwonjezera apo, Yehu anapitiriza kupha onse a m’nyumba ya Ahabu amene anatsala ku Yezereeli, amuna ake onse olemekezeka,+ anzake, ndi ansembe ake,+ mpaka onse anatha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena