Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 21:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Munthu wa m’banja la Ahabu wofera mumzinda, agalu adzamudya, ndipo wofera kuthengo, mbalame zam’mlengalenga zidzamudya.+

  • 1 Mafumu 21:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndithu ndidzachititsa nyumba yako kukhala ngati nyumba ya Yerobowamu+ mwana wa Nebati ndiponso nyumba ya Basa+ mwana wa Ahiya, chifukwa chakuti wandikwiyitsa n’kuchimwitsanso Isiraeli.’+

  • 2 Mafumu 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ukaphe anthu a m’nyumba ya mbuye wako Ahabu, kuti ine ndibwezere+ magazi a atumiki anga aneneri ndiponso magazi a atumiki onse a Yehova amene Yezebeli anapha.+

  • 2 Mafumu 9:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Anthuwo atabwerera kwa Yehu kukamuuza, iye anati: “Amenewo ndi mawu a Yehova amene analankhula kudzera+ mwa mtumiki wake Eliya wa ku Tisibe, kuti, ‘M’munda wa ku Yezereeli, agalu adzadya mnofu wa Yezebeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena