Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 12:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsopano wansembe Yehoyada anatenga bokosi+ n’kuboola kachibowo pachivundikiro chake. Kenako anaika bokosilo pambali pa guwa lansembe kumanja, munthu akamalowa m’nyumba ya Yehova. Ansembe omwe anali alonda a pakhomo+ anaika m’bokosilo ndalama zonse+ zimene anthu anali kubweretsa kunyumba ya Yehova.

  • Maliko 12:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndiyeno anakhala pansi moyang’anana ndi moponyamo zopereka+ ndipo anali kuona mmene khamu la anthu linali kuponyera ndalama moponya zoperekamo. Anthu ambiri olemera anali kuponyamo makobidi ambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena