Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 16:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pa nthawiyo, Rezini mfumu ya Siriya anabwezeretsa mzinda wa Elati+ ku Edomu. Kenako anachotsa Ayuda mu Elati ndipo Aedomu analowa n’kumakhalamo. Iwo akukhalabe komweko mpaka lero.

  • 2 Mbiri 24:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Gulu lankhondo la Siriyalo linalowa m’dzikolo ndi amuna ochepa,+ koma Yehova anapereka m’manja mwawo gulu lankhondo lalikulu kwambiri+ popeza iwo anasiya Yehova Mulungu wa makolo awo. Asiriyawo anaperekanso chiweruzo kwa Yehoasi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena