Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “‘Kenako azipha ng’ombe yaing’onoyo pamaso pa Yehova. Ndiyeno ana a Aroni, ansembe,+ azibweretsa magazi ake ndi kuwawaza mozungulira paguwa lansembe,+ limene lili pakhomo la chihema chokumanako.

  • Levitiko 4:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ena mwa magaziwo aziwapaka panyanga za guwa lansembe+ limene lili pamaso pa Yehova, m’chihema chokumanako. Magazi ena onse aziwathira pansi pa guwa lansembe zopsereza,+ limene lili pakhomo la chihema chokumanako.

  • Aheberi 9:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndipo anawazanso magazi aja pachihema+ ndi paziwiya zonse zogwiritsa ntchito potumikira ena.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena