Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 25:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ana onsewa anali kuyang’aniridwa ndi bambo awo poimba nyimbo m’nyumba ya Yehova. Ankaimba nyimbozo ndi zinganga,+ zoimbira za zingwe,+ ndi azeze,+ pochita utumiki wa panyumba ya Mulungu woona.

      Koma Asafu, Yedutuni, ndi Hemani anali kuyang’aniridwa ndi mfumu.+

  • 2 Mbiri 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mfumuyo inapanga masitepe a nyumba ya Yehova ndi a nyumba ya mfumu+ pogwiritsira ntchito matabwa a m’bawawo.+ Inapanganso azeze+ ndi zoimbira za zingwe+ n’kupatsa oimba.+ Zinthu zamtundu umenewu zinali zisanaonekepo m’dziko la Yuda.

  • Salimo 149:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Atamande dzina lake mwa kuvina.+

      Amuimbire nyimbo zomutamanda ndi maseche ndi zeze,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena