Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 29:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Koma ansembe+ anali ochepa kwambiri ndipo sanathe kusenda nyama zonse za nsembe zopsereza.+ Choncho abale awo+ Alevi anawathandiza mpaka ntchitoyo inatha+ ndiponso kufikira pamene ansembewo anadziyeretsa,+ popeza Alevi ankafunitsitsa kudziyeretsa kuposa ansembe.+

  • 2 Mbiri 35:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno anauza Alevi, alangizi+ a Isiraeli yense, omwe anali oyera kwa Yehova, kuti: “Ikani Likasa lopatulika+ m’nyumba+ imene Solomo mwana wa Davide mfumu ya Isiraeli anamanga. Lisakhalenso katundu wolemera pamapewa anu.+ Tsopano tumikirani+ Yehova Mulungu wanu ndi anthu ake Aisiraeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena