Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 25:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Patapita masiku 10, Yehova anakantha+ Nabala ndipo anafa.

  • 2 Samueli 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako Natani anapita kunyumba kwake.

      Ndiyeno Yehova anakantha+ mwana amene mkazi wa Uriya anaberekera Davide, moti mwanayo anayamba kudwala.

  • 1 Mafumu 14:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yerobowamu analamulira zaka 22, kenako anagona pamodzi ndi makolo ake,+ ndipo Nadabu+ mwana wake anayamba kulamulira m’malo mwake.

  • Machitidwe 12:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Nthawi yomweyo mngelo wa Yehova anamukantha,+ chifukwa sanapereke ulemerero kwa Mulungu.+ Ndipo anadyedwa ndi mphutsi n’kumwalira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena