Yoswa 23:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Tsopano Yoswa anali atakalamba ndiponso anali ndi zaka zambiri.+ Apa n’kuti patapita masiku ambiri kuchokera pamene Yehova anapatsa Aisiraeli mpumulo+ pakati pa adani awo onse owazungulira. 2 Mbiri 15:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Ayuda onse anayamba kusangalala+ chifukwa cha zimene analumbirazo popeza analumbira ndi mtima wawo wonse, komanso chifukwa chakuti anafunafuna Mulungu mokondwa kwambiri moti iye analola kuti amupeze.+ Choncho Yehova anapitiriza kuwapatsa mpumulo pakati pa adani awo onse owazungulira.+ Salimo 46:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Akuletsa nkhondo mpaka kumalekezero a dziko lapansi.+Wathyola uta ndi kuduladula mkondo.+Ndipo watentha magaleta pamoto.+ Miyambo 16:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Yehova akasangalala ndi njira za munthu,+ amachititsa ngakhale adani a munthuyo kukhala naye pa mtendere.+
23 Tsopano Yoswa anali atakalamba ndiponso anali ndi zaka zambiri.+ Apa n’kuti patapita masiku ambiri kuchokera pamene Yehova anapatsa Aisiraeli mpumulo+ pakati pa adani awo onse owazungulira.
15 Ayuda onse anayamba kusangalala+ chifukwa cha zimene analumbirazo popeza analumbira ndi mtima wawo wonse, komanso chifukwa chakuti anafunafuna Mulungu mokondwa kwambiri moti iye analola kuti amupeze.+ Choncho Yehova anapitiriza kuwapatsa mpumulo pakati pa adani awo onse owazungulira.+
9 Akuletsa nkhondo mpaka kumalekezero a dziko lapansi.+Wathyola uta ndi kuduladula mkondo.+Ndipo watentha magaleta pamoto.+
7 Yehova akasangalala ndi njira za munthu,+ amachititsa ngakhale adani a munthuyo kukhala naye pa mtendere.+