Ezara 1:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Ndiyeno atsogoleri+ a mabanja a fuko la Yuda, la Benjamini, ansembe, ndi Alevi, aliyense amene Mulungu woona analimbikitsa mtima wake,+ ananyamuka kuti apite kukamanganso nyumba ya Yehova,+ yomwe inali ku Yerusalemu. Ezara 2:36 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 Ansembe:+ Ana a Yedaya,+ a m’nyumba ya Yesuwa,+ 973.
5 Ndiyeno atsogoleri+ a mabanja a fuko la Yuda, la Benjamini, ansembe, ndi Alevi, aliyense amene Mulungu woona analimbikitsa mtima wake,+ ananyamuka kuti apite kukamanganso nyumba ya Yehova,+ yomwe inali ku Yerusalemu.