3 Pa nthawi imeneyo Tatenai+ bwanamkubwa wa kutsidya lina la Mtsinje,*+ Setara-bozenai, ndi anzawo anabwera kwa Ayudawo n’kudzawafunsa kuti: “Kodi ndani wakulamulani kuti mumange nyumbayi ndi kumaliza khoma* lamatabwali?”+
6 “Tsopano inu Tatenai+ bwanamkubwa wa kutsidya lina la Mtsinje,*+ Setara-bozenai+ ndi anzanu ndiponso abwanamkubwa aang’ono+ amene ali kutsidya lina la Mtsinje, musakasokoneze kumeneko.+