Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 7:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ezara ameneyu ananyamuka n’kuchoka ku Babulo. Iye anali katswiri wodziwa kukopera+ chilamulo cha Mose,+ chimene Yehova Mulungu wa Isiraeli anapereka. Chotero mfumu inamupatsa zopempha zake zonse chifukwa dzanja la Yehova Mulungu wake linali pa iye.+

  • Nehemiya 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho Ezara wansembe+ anabweretsa chilamulo pamaso pa mpingo+ wa amuna komanso akazi ndi ana onse amene akanatha kumvetsera ndi kuzindikira+ zimene zinali kunenedwa. Limeneli linali tsiku loyamba la mwezi wa 7.+

  • Nehemiya 12:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Anthu amenewa anakhalapo m’masiku a Yoyakimu+ mwana wa Yesuwa+ amene anali mwana wa Yozadaki,+ komanso m’masiku a Nehemiya+ amene anali bwanamkubwa, ndi Ezara+ amene anali wansembe komanso wokopera Malemba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena