Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno Meremoti+ mwana wamwamuna wa Uliya,+ mwana wamwamuna wa Hakozi, anakonza mpandawo kuchokera pamene ana aamuna a Haseneya analekezera. Kenako, Mesulamu+ mwana wamwamuna wa Berekiya, mwana wamwamuna wa Mesezabele, anakonza mpandawo kuchokera pamene Meremoti analekezera. Kenako, Zadoki mwana wamwamuna wa Baana, anakonza mpandawo kuchokera pamene Mesulamu analekezera.

  • Nehemiya 3:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kenako, Meremoti mwana wamwamuna wa Uliya,+ mwana wamwamuna wa Hakozi, anakonza gawo lina la mpandawo kuchokera pachipata cha nyumba ya Eliyasibu mpaka polekezera nyumbayo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena