Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 34:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Maso a Yehova ali pa olungama,+

      Ndipo makutu ake amamva kufuula kwawo kopempha thandizo.+

  • Salimo 55:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Umutulire Yehova nkhawa zako,+

      Ndipo iye adzakuchirikiza.+

      Sadzalola kuti wolungama agwedezeke.+

  • Salimo 62:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Mukhulupirireni nthawi zonse, anthu inu.+

      Mukhuthulireni za mumtima mwanu.+

      Mulungu ndiye pothawirapo pathu.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 115:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iwe Isiraeli, khulupirira Yehova.+

      Iye ndiye thandizo lako ndi chishango chako.+

  • Miyambo 29:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kuopa anthu n’kumene kumatchera msampha,+ koma wokhulupirira Yehova adzatetezedwa.+

  • Aroma 16:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iwo anaika miyoyo+ yawo pachiswe chifukwa cha moyo wanga, ndipo si ine ndekha amene ndikuwayamikira,+ komanso mipingo yonse ya anthu a mitundu ina.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena