Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mudzamva kuchonderera kwa anthu ofatsa,+ inu Yehova.

      Mudzakonzekeretsa mitima yawo.+

      Mudzatchera khutu lanu,+

  • Salimo 18:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pa nthawi ya zowawa zanga ndinaitana Yehova,

      Ndinafuulira Mulungu wanga kuti andithandize.+

      Iye anamva mawu anga ali m’kachisi wake.+

      Pamenepo makutu ake anamva kulira kwanga kopempha thandizo.+

  • Salimo 94:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kodi amene anakupatsani makutu, sangamve?+

      Kapena amene anapanga maso, sangaone?+

  • Yesaya 59:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Dzanja la Yehova silinafupike moti n’kulephera kupulumutsa,+ komanso khutu lake silinagonthe moti n’kulephera kumva.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena