Genesis 21:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Pamenepo Mulungu anamva mawu a mnyamatayo,+ ndipo mngelo wa Mulungu analankhula ndi Hagara kuchokera kumwamba+ kuti: “Kodi watani Hagara? Usaope, Mulungu wamva mawu a mnyamatayo pomwe wagonapo. Ekisodo 4:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Pamenepo Yehova anamuuza kuti: “Anapatsa munthu pakamwa ndani, kapena ndani amapanga munthu wosalankhula, wogontha, woona kapena wakhungu? Kodi si ine, Yehova?+ Salimo 55:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Mulungu amene wakhala pampando wachifumu kuyambira kalekale,+Adzandimvera ndipo adzawayankha,+ [Seʹlah.]Anthu osafuna kusintha makhalidwe awo oipa,+Ndiponso amene saopa Mulungu.+ Salimo 69:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Pakuti Yehova akumvetsera osauka,+Ndipo sadzanyoza anthu ake amene ali m’ndende.+
17 Pamenepo Mulungu anamva mawu a mnyamatayo,+ ndipo mngelo wa Mulungu analankhula ndi Hagara kuchokera kumwamba+ kuti: “Kodi watani Hagara? Usaope, Mulungu wamva mawu a mnyamatayo pomwe wagonapo.
11 Pamenepo Yehova anamuuza kuti: “Anapatsa munthu pakamwa ndani, kapena ndani amapanga munthu wosalankhula, wogontha, woona kapena wakhungu? Kodi si ine, Yehova?+
19 Mulungu amene wakhala pampando wachifumu kuyambira kalekale,+Adzandimvera ndipo adzawayankha,+ [Seʹlah.]Anthu osafuna kusintha makhalidwe awo oipa,+Ndiponso amene saopa Mulungu.+