Deuteronomo 33:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Mulungu wakale lomwe ndiwo malo ako obisalamo,+Ndipo iwe uli m’manja amene adzakhalapo mpaka kalekale.+Adzapitikitsa mdani pamaso pako,+Ndipo adzanena kuti, ‘Awononge!’+ Salimo 90:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Mapiri asanabadwe,+Kapena musanakhazikitse dziko lapansi+ ndi malo okhalapo anthu,*+Inu ndinu Mulungu kuyambira kalekale mpaka kalekale.+ Yeremiya 10:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Koma Yehova ndi Mulungu woonadi.+ Iye ndi Mulungu wamoyo+ ndipo ndi Mfumu mpaka kalekale.+ Dziko lapansi lidzagwedezeka ndi mkwiyo wake,+ ndipo palibe mitundu ya anthu imene idzalimbe pamene iye akuidzudzula.+
27 Mulungu wakale lomwe ndiwo malo ako obisalamo,+Ndipo iwe uli m’manja amene adzakhalapo mpaka kalekale.+Adzapitikitsa mdani pamaso pako,+Ndipo adzanena kuti, ‘Awononge!’+
2 Mapiri asanabadwe,+Kapena musanakhazikitse dziko lapansi+ ndi malo okhalapo anthu,*+Inu ndinu Mulungu kuyambira kalekale mpaka kalekale.+
10 Koma Yehova ndi Mulungu woonadi.+ Iye ndi Mulungu wamoyo+ ndipo ndi Mfumu mpaka kalekale.+ Dziko lapansi lidzagwedezeka ndi mkwiyo wake,+ ndipo palibe mitundu ya anthu imene idzalimbe pamene iye akuidzudzula.+