Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 107:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ena anali kukhala mu mdima, mu mdima wandiweyani,+

      Anali akaidi osautsika ndi omangidwa maunyolo,+

  • Salimo 146:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iye ndi Woperekera chiweruzo anthu ochitiridwa chinyengo,+

      Wopereka chakudya kwa anthu anjala.+

      Yehova amamasula anthu omangidwa.+

  • Yesaya 61:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 61 Mzimu wa Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, uli pa ine,+ pakuti Yehova wandidzoza+ kuti ndikanene uthenga wabwino kwa anthu ofatsa.+ Wandituma kuti ndikamange zilonda za anthu osweka mtima,+ ndikalengeze za ufulu kwa anthu ogwidwa ndi kutengedwa kupita kudziko lina,+ ndiponso ndikatsegule maso a akaidi.+

  • Zekariya 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Koma mkazi iwe, chifukwa cha magazi a pangano limene unapangana ndi ine,+ ndidzatulutsa akaidi ako+ m’dzenje lopanda madzi.

  • Machitidwe 5:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Koma usiku, mngelo wa Yehova+ anatsegula zitseko za ndendeyo+ ndi kuwatulutsa, ndipo anawauza kuti:

  • Machitidwe 12:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mwadzidzidzi, mngelo wa Yehova anaimirira+ chapafupi, ndipo kuwala kunaunika m’chipinda cha ndendecho. Kenako mngeloyo anadzutsa Petulo mwa kumugunda m’nthiti,+ n’kunena kuti: “Dzuka msanga!” Pamenepo maunyolo amene anamumanga nawo manjawo anagwa pansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena