2 Mbiri 33:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Pomalizira pake Yehova anawabweretsera+ akuluakulu a asilikali a mfumu ya Asuri.+ Iwo anagwira Manase akubisala m’dzenje.+ Atatero anam’manga+ ndi zomangira ziwiri zamkuwa n’kupita naye ku Babulo. Yobu 36:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Anthu akamangidwa m’matangadza,+Amagwidwa ndi zingwe za masautso. Salimo 105:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Kumeneko anasautsa mapazi ake ndi matangadza,+Anam’manga ndi maunyolo.+ Salimo 149:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Ndiponso kuti amange mafumu awo maunyolo,+Ndi kumanga anthu awo olemekezeka m’matangadza achitsulo. Mabuku a Chichewa (1974-2025) Tulukani Lowani Chichewa Tumizirani Ena Zimene Mumakonda Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania Zoyenera Kutsatira Nkhani Yosunga Chinsinsi Privacy Settings JW.ORG Lowani Tumizirani Ena Tumizirani Wina pa Imelo
11 Pomalizira pake Yehova anawabweretsera+ akuluakulu a asilikali a mfumu ya Asuri.+ Iwo anagwira Manase akubisala m’dzenje.+ Atatero anam’manga+ ndi zomangira ziwiri zamkuwa n’kupita naye ku Babulo.
18 Kumeneko anasautsa mapazi ake ndi matangadza,+Anam’manga ndi maunyolo.+ Salimo 149:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Ndiponso kuti amange mafumu awo maunyolo,+Ndi kumanga anthu awo olemekezeka m’matangadza achitsulo.
8 Ndiponso kuti amange mafumu awo maunyolo,+Ndi kumanga anthu awo olemekezeka m’matangadza achitsulo.