Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Nyale ya Mulungu inali isanazimitsidwe, ndipo Samueli anali atagona m’kachisi+ wa Yehova, mmene munali likasa la Mulungu.

  • 2 Samueli 22:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Pa nthawi ya zowawa zanga ndinaitana Yehova,+

      Ndinaitana Mulungu wanga.+

      Pamenepo iye anamva mawu anga ali m’kachisi wake,+

      Makutu ake anamva kulira kwanga kopempha thandizo.+

  • 1 Mbiri 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Motero analowetsa+ likasa la Mulungu woona muhema limene Davide anamanga, n’kuika likasalo pamalo ake muhemalo.+ Kenako iwo anapereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano kwa Mulungu woona.+

  • Salimo 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova ali m’kachisi wake wopatulika.+

      Yehova, mpando wake wachifumu uli kumwamba.+

      Maso ake amaona, maso ake owala amasanthula+ ana a anthu.

  • Yona 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Pamene ndinalefuka kwambiri,+ ndinakumbukira Yehova.+

      Ndipo pemphero langa linafika kwa inu, m’kachisi wanu woyera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena