Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 77:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndidzakumbukira zochita za Ya,+

      Ndithu ndidzakumbukira ntchito yanu yodabwitsa yakale.+

  • Salimo 143:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndakumbukira masiku akale.+

      Ndasinkhasinkha zochita zanu zonse,+

      Ndipo ndakhala ndikuganizira ntchito ya manja anu ndi mtima wonse.+

  • 2 Akorinto 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ngakhalenso m’mitima mwathu, tinali kumva ngati talandira chiweruzo cha imfa. Zinatero kuti tisakhale ndi chikhulupiriro mwa ife tokha,+ koma mwa Mulungu amene amaukitsa akufa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena