Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye ndi Thanthwe, ndipo ntchito yake ndi yangwiro,+

      Njira zake zonse ndi zolungama.+

      Mulungu wokhulupirika,+ amene sachita chosalungama.+

      Iye ndi wolungama ndi wowongoka.+

  • Salimo 19:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mawu a pakamwa panga ndi kusinkhasinkha kwa mtima wanga,+

      Zikukondweretseni, inu Yehova, Thanthwe langa+ ndi Wondiwombola.+

  • Salimo 64:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Anthu onse adzachita mantha,+

      Ndipo adzanena za ntchito za Mulungu,+

      Iwo adzamvetsa bwino ntchito zake.+

  • Salimo 77:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndidzasinkhasinkha za ntchito zanu zonse,+

      Ndipo ndiziganizira zochita zanu.+

  • Salimo 90:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ntchito zanu zionekere kwa atumiki anu,+

      Ndipo ulemerero wanu uonekere pa ana awo.+

  • Salimo 111:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Zochita zake+ n’zaulemerero ndi ulemu,+

      ו [Waw]

      Ndipo chilungamo chake chidzakhalapobe kwamuyaya.+

  • Afilipi 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chomalizira abale, zinthu zilizonse zoona, zilizonse zofunika kwambiri, zilizonse zolungama, zilizonse zoyera,+ zilizonse zachikondi, zilizonse zoyamikirika, khalidwe labwino lililonse, ndi chilichonse chotamandika, pitirizani kuganizira zimenezi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena