Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Dzanja lanu lamanja, inu Yehova, likusonyeza kupambana kwa mphamvu zake.+

      Dzanja lanu lamanja, inu Yehova, limaphwanya mdani.+

  • 1 Mbiri 16:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ulemu ndi ulemerero zili pamaso pake,+

      Pokhala pake pali mphamvu ndi chimwemwe.+

  • Yobu 40:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tadziveka ukulu+ ndiponso kukwezeka,+

      Ndipo uvale ulemu+ ndi ulemerero.+

  • Salimo 145:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kuti ana a anthu adziwe za ntchito zanu zamphamvu+

      Ndi kukula kwa ulemerero wa ufumu wanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena