Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 98:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova wachititsa chipulumutso chake kudziwika.+

      Chilungamo chake wachisonyeza ku mitundu ya anthu.+

  • Salimo 103:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma Yehova adzapitiriza kusonyeza kukoma mtima kwake kosatha mpaka kalekale,+

      Kwa anthu amene amamuopa.+

      Ndipo adzapitiriza kusonyeza chilungamo chake kwa ana a ana awo.+

  • Yesaya 5:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yehova wa makamu adzakwezeka kudzera m’chiweruzo,+ ndipo Mulungu woona, Woyera,+ adzadziyeretsa kudzera m’chilungamo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena