Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 16:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndaika Yehova patsogolo panga nthawi zonse.+

      Popeza kuti ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.+

  • Salimo 37:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ngakhale atapunthwa, sadzagweratu,+

      Pakuti Yehova wamugwira dzanja.+

  • Salimo 62:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iye ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa, malo anga okwezeka ndiponso achitetezo.+

      Sindidzagwedezeka kwambiri.+

  • Salimo 121:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Iye sangalole kuti phazi lako lipunthwe.+

      Amene amakuyang’anira sangawodzere.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena