Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Atumiki onse a mfumu ndi anthu a m’zigawo za mfumu akudziwa kuti mfumu ili ndi lamulo limodzi lokhudza mwamuna kapena mkazi aliyense wokaonekera kwa iye m’bwalo lamkati+ asanaitanidwe. Lamuloli+ ndi lakuti aphedwe. Koma ngati mfumu yamuloza ndi ndodo yachifumu ya golide, pamenepo adzakhala ndi moyo.+ Ndiye ine sindinaitanidwe kukaonekera kwa mfumu kwa masiku 30 tsopano.”

  • Esitere 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako mfumu inati: “Kodi m’bwalo muli ndani?” Tsopano Hamani anali atalowa m’bwalo lakunja+ kwa nyumba ya mfumu kudzauza mfumu kuti apachike Moredekai pamtengo+ umene anamukonzera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena