Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pamenepo mkazi wake Zeresi ndi anzake onsewo anamuuza kuti: “Mukonzetse mtengo+ wotalika mikono* 50. Ndiyeno m’mawa+ mukauze mfumu kuti apachike Moredekai pamtengowo.+ Mukatero mupite kuphwando ndi mfumu muli wosangalala.” Zimenezi zinaoneka zosangalatsa+ kwa Hamani, choncho anakonzetsa mtengowo.+

  • Esitere 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Haribona,+ mmodzi mwa nduna za panyumba ya mfumu+ amene anali pamaso pa mfumu anati: “Palinso mtengo+ umene Hamani anapangira Moredekai, amene analankhula zabwino za mfumu.+ Mtengowu uli m’nyumba ya Hamani ndipo ndi wotalika mikono 50.” Pamenepo mfumu inati: “Amuna inu, kam’pachikeni pamtengo umenewo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena