Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 7:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Nyamukani, inu Yehova, mu mkwiyo wanu.+

      Imirirani ndi kukhaulitsa amene andisonyeza mkwiyo ndi kundichitira zoipa.+

      Dzukani ndi kundithandiza,+ pakuti mwalamula kuti chiweruzo chiperekedwe.+

  • Salimo 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Anthu a mitundu ina agwera m’dzenje limene anakumba okha.+

      Phazi lawo lakodwa mu ukonde+ umene anatchera okha.+

  • Salimo 35:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Awonongeke pamene iwo sakuyembekezera,+

      Akodwe mu ukonde umene atchera okha.+

      Agweremo ndi kuwonongeka.+

  • Salimo 73:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Haa! M’kanthawi kochepa, iwo akhala chinthu chodabwitsa.+

      Afika pamapeto awo ndipo atha chifukwa cha masoka owagwera modzidzimutsa!

  • Miyambo 11:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kulungama kwa anthu owongoka mtima n’kumene kudzawapulumutse,+ koma anthu ochita zinthu mwachinyengo adzagwidwa ndi zolakalaka zawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena