Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pamenepo mkazi wake Zeresi ndi anzake onsewo anamuuza kuti: “Mukonzetse mtengo+ wotalika mikono* 50. Ndiyeno m’mawa+ mukauze mfumu kuti apachike Moredekai pamtengowo.+ Mukatero mupite kuphwando ndi mfumu muli wosangalala.” Zimenezi zinaoneka zosangalatsa+ kwa Hamani, choncho anakonzetsa mtengowo.+

  • Esitere 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno Hamani anafotokozera Zeresi+ mkazi wake ndi anzake onse chilichonse chimene chinam’chitikira. Pamenepo amuna anzeru+ amene anali kum’tumikira ndi Zeresi mkazi wake anati: “Ngati n’zoona kuti Moredekai amene iwe wayamba kugonja pamaso pake ndi Myuda, sudzamugonjetsa koma udzagonja ndithu pamaso pake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena