Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pa tsiku la 7, pamene mtima wa mfumu unali kukondwera ndi vinyo,+ mfumu inauza Mehumani, Bizita, Haribona,+ Bigita, Abagata, Zetara ndi Karikasi, nduna 7 za panyumba ya mfumu zimene zinali kutumikira+ Mfumu Ahasiwero,

  • Esitere 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Alangizi amene anali pafupi kwambiri ndi mfumu anali Karisena, Setara, Adimata, Tarisi, Meresi, Marisena ndi Memukani, akalonga 7+ a Perisiya ndi Mediya, amene nthawi zonse anali kufika pamaso pa mfumu+ komanso anali ndi maudindo akuluakulu mu ufumuwo.)

  • Esitere 6:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pamene anali kukambirana naye zimenezi, nduna za panyumba ya mfumu zinafika, ndipo mofulumira+ zinatenga Hamani ndi kupita naye kuphwando+ limene Esitere anakonza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena