Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 7:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndawaza pabedi panga zonunkhiritsa za mule, aloye ndi sinamoni.+

  • Nyimbo ya Solomo 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Kodi chinthu chikuchokera kuchipululuchi n’chiyani, chooneka ngati utsi wokwera m’mwamba, chonunkhira mafuta a mule, lubani,*+ ndi mtundu uliwonse wa zonunkhira za ufa za munthu wamalonda?”+

  • Luka 7:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Koma mayi wina amene anali wodziwika mumzindawo kuti ndi wochimwa, anamva kuti Yesu akudya chakudya m’nyumba ya Mfarisi. Choncho anapita komweko ndi botolo lopangidwa ndi mwala wa alabasitala,+ muli mafuta onunkhira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena