Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 12:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iyetu amagwetsa zinthu kuti zisamangidwe,+

      Zimene iye watseka, palibe munthu amene angazitsegule.+

  • Yobu 19:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye watchinga njira yanga ndi mpanda wamiyala+ mwakuti sindingathe kudutsa.

      Ndiponso waika mdima panjira zanga.+

  • Maliro 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Watsekereza njira zanga ndi miyala yosema.+ Wachititsa njira zanga kukhala zovuta kuyendamo.+

  • Hoseya 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Tsopano ine ndikutsekereza njira yake ndi mpanda waminga, ndipo ndidzamumangira mpanda wamiyala+ ndi kumutsekereza kuti asapeze njira zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena