Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 102:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Masiku a moyo wanga ali ngati chithunzithunzi chimene chimazimiririka dzuwa likalowa,+

      Ndipo ndauma ngati udzu.+

  • Salimo 103:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Masiku a moyo wa munthu ali ngati masiku a udzu wobiriwira.+

      Iye amaphuka ngati mmene duwa lakutchire limaphukira.+

  • Salimo 144:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Munthu amafanana ndi mpweya wotuluka m’mphuno.+

      Masiku ake ali ngati mthunzi wongodutsa.+

  • Yakobo 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mumatero chonsecho simukudziwa kuti moyo wanu udzakhala wotani mawa.+ Pakuti ndinu nkhungu yongoonekera kanthawi kenako n’kuzimiririka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena