Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:73
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  73 Manja anu anandipanga, ndipo anandiumba.+

      Ndithandizeni kukhala wozindikira, kuti ndiphunzire malamulo anu.+

  • Salimo 139:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Inu munapanga impso zanga,+

      Ndipo munali kunditchinga m’mimba mwa mayi anga.+

  • Salimo 139:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mafupa anga sanali obisika kwa inu+

      Pamene munali kundipanga m’malo obisika,+

      Pamene munali kundiwomba ngati nsalu m’malo apansi kwambiri+ padziko lapansi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena