Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 10:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Manja anu omwe ndi amene anandiumba, ndipo anandipanga+

      Kuzungulira thupi langa lonse, koma tsopano mukufuna kundimeza.

  • Salimo 100:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.+

      Iye ndi amene anatipanga, sitinadzipange tokha.+

      Ndife anthu ake ndi nkhosa zimene akuweta.+

  • Salimo 138:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova adzakwaniritsa zolinga zimene ali nazo pa ine.+

      Inu Yehova, kukoma mtima kwanu kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+

      Musasiye ntchito ya manja anu.+

  • Salimo 139:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndidzakutamandani chifukwa munandipanga modabwitsa ndipo zimenezi zimandichititsa mantha.+

      Ntchito zanu ndi zodabwitsa,+

      Ndipo ine ndimadziwa bwino zimenezi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena