Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 49:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Awatsogolera ku Manda ngati nkhosa zopita kokaphedwa.+

      Imfa idzakhala m’busa wawo.+

      Ndipo m’mawa anthu owongoka mtima adzawalamulira.+

      Matupi awo adzawonongeka.+

      Aliyense wa iwo malo ake okhala ndi ku Manda, osati malo okwezeka.+

  • Salimo 55:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Chiwonongeko chiwagwere!+

      Atsikire ku Manda ali amoyo.+

      Pakuti kulikonse kumene apita, zinthu zoipa zimakhala mumtima mwawo.+

  • Luka 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma Mulungu anamuuza kuti, ‘Wopanda nzeru iwe, usiku womwe uno moyo wako adzaufuna.+ Nanga chuma chimene waunjikachi chidzakhala cha ndani?’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena