Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno Yobu anatenga phale loti azidzikanda nalo ndipo anali kukhala paphulusa.+

  • Yobu 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kenako anakhala+ naye limodzi pansi masiku 7 usana ndi usiku, ndipo palibe amene anali kumulankhula chilichonse popeza iwo anaona kuti ululu+ wake unali waukulu kwambiri.

  • Yobu 7:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndikagona ndimanena kuti, ‘Kodi ndidzuka nthawi yanji?’+

      Kukada ndimangokhalira kutembenukatembenuka mpaka m’mawa kuli mbuu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena