Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 12:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kodi khutu si paja limasiyanitsa mawu+

      Ngati mmene m’kamwa+ mumasiyanitsira kakomedwe ka chakudya?

  • Machitidwe 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma anthu a ku Bereya anali a mtima wofuna kuphunzira kuposa a ku Tesalonika aja. Iwowa analandira mawu a Mulungu ndi chidwi chachikulu kwambiri, ndipo tsiku ndi tsiku anali kufufuza+ Malemba+ mosamala kuti atsimikizire ngati zimene anamvazo zinalidi zoona.+

  • Chivumbulutso 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ali ndi makutu amve zimene mzimu+ ukunena ku mipingo kuti: Wopambana pa nkhondo,+ ndidzamulola kudya za mumtengo wa moyo,+ umene uli m’paradaiso wa Mulungu.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena